Machitidwe a Atumwi 7:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo zitapita zaka makumi anai, anamuonekera mngelo m'chipululu cha Sinai, m'lawi la moto wa m'chitsamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo zitapita zaka makumi anai, anamuonekera mngelo m'chipululu cha Sinai, m'lawi la moto wa m'chitsamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 “Tsono patapita zaka makumi anai, mngelo adaonekera Mose ku chipululu cha ku phiri la Sinai, m'malaŵi a moto pa chitsamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Ndipo patapita zaka makumi anayi mngelo anaonekera kwa Mose mʼmalawi amoto pa chitsamba mʼchipululu pafupi ndi Phiri la Sinai. Onani mutuwo |