Machitidwe a Atumwi 7:31 - Buku Lopatulika31 Koma Mose pakuona, anazizwa pa choonekacho; ndipo pakuyandikira iye kukaona, kunadza mau a Ambuye, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma Mose pakuona, anazizwa pa choonekacho; ndipo pakuyandikira iye kukaona, kunadza mau a Ambuye, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Mose ataona zimenezi adazizwa, ndipo adasendera pafupi kuti aonetsetse. Pamenepo adamva mau a Chauta akuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Iye ataona zimenezi, anadabwa. Akupita kuti akaonetsetse pafupi, Mose anamva mawu a Ambuye: Onani mutuwo |