Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo Mose anathawa pa mau awa, nakhala mlendo m'dziko la Midiyani; kumeneko anabala ana aamuna awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo Mose anathawa pa mau awa, nakhala mlendo m'dziko la Midiyani; kumeneko anabala ana amuna awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Pamene Mose adamva mau ameneŵa, adathaŵa namakakhala ku chilendo ku dziko la Midiyani. Kumeneko adabereka ana aamuna aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Mose atamva mawu awa anathawira ku Midiyani, kumene anakhala mlendo ndipo anabereka ana amuna awiri.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:29
3 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa