Machitidwe a Atumwi 7:3 - Buku Lopatulika3 nati kwa iye, Tuluka kudziko lako ndi kwa abale ako, ndipo tiye kudziko limene ndidzakusonyeza iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nati kwa iye, Tuluka kudziko lako ndi kwa abale ako, ndipo tiye kudziko limene ndidzakusonyeza iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adamuuza kuti, ‘Tuluka m'dziko lako, uŵasiye abale ako, ubwere ku dziko limene ndidzakusonyeza.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu anati, ‘Tuluka mʼdziko lako, siya abale ako, ndipo pita ku dziko limene ndidzakusonyeza.’ Onani mutuwo |