Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:4 - Buku Lopatulika

4 Pamenepo anatuluka m'dziko la Akaldeya namanga mu Harani: ndipo, kuchokera kumeneko, atamwalira atate wake, Mulungu anamsuntha alowe m'dziko lino, m'mene mukhalamo tsopano;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamenepo anatuluka m'dziko la Akaldeya namanga m'Harani: ndipo, kuchokera kumeneko, atamwalira atate wake, Mulungu anamsuntha alowe m'dziko lino, m'mene mukhalamo tsopano;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono adatulukadi m'dziko la Akaldeya nakakhala ku Harani. Bambo wake atamwalira, Mulungu adamchotsa kumeneko, nakamufikitsa ku dziko lino kumene inu mukukhala tsopano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 “Ndipo iye anatulukadi mʼdziko la Akaldeya ndi kukakhala ku Harani. Atamwalira abambo ake, Mulungu anamuchotsa kumeneko ndi kumubweretsa mʼdziko lino limene inu mukukhalamo tsopano.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa iye, Ine ndine Yehova amene ndinatulutsa iwe mu Uri wa kwa Akaldeya, kuti ndikupatse iwe dziko limeneli likhale lakolako.


Ndani anautsa wina wochokera kum'mawa, amene amuitana m'chilungamo, afike pa phazi lake? Iye apereka amitundu patsogolo pake, namlamuliritsa mafumu; nawapereka monga fumbi kulupanga lake, monga chiputu chouluzidwa ku uta wake.


iwe amene ndinakuwira iwe zolimba kuchokera ku malekezero a dziko lapansi, ndi kukuitana iwe kuchokera m'ngodya zake, ndipo ndinati kwa iwe, Ndiwe mtumiki wanga ndakusankha, sindinakutaye kunja;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa