Machitidwe a Atumwi 7:23 - Buku Lopatulika23 Koma pamene zaka zake zinafikira ngati makumi anai, kunalowa mumtima mwake kuzonda abale ake ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma pamene zaka zake zinafikira ngati makumi anai, kunalowa mumtima mwake kuzonda abale ake ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 “Pamene zaka zake zidafikira makumi anai, adaganiza zokayendera abale ake, Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 “Mose ali ndi zaka makumi anayi, anaganizira zokayendera abale ake Aisraeli. Onani mutuwo |