Machitidwe a Atumwi 7:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Mose anaphunzira nzeru zonse za Aejipito; nali wamphamvu m'mau ake ndi m'ntchito zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Mose anaphunzira nzeru zonse za Aejipito; nali wamphamvu m'mau ake ndi m'ntchito zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Motero Mose adaphunzira nzeru zonse za anthu a ku Ejipito, ndipo mau ake ndi ntchito zake zinali zamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mose anaphunzira nzeru zonse za Aigupto, ndipo anali wamphamvu mʼmawu ndi ntchito zake. Onani mutuwo |