Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:21 - Buku Lopatulika

21 ndipo pakutayika iye, anamtola mwana wamkazi wa Farao, namlera akhale mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 ndipo pakutayika iye, anamtola mwana wamkazi wa Farao, namlera akhale mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 koma atamsiya pamtsinje paja, mwana wamkazi wa Farao adamtola, namlera ngati mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Atakamutaya, mwana wamkazi wa Farao anamutola nakamulera ngati mwana wake.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:21
3 Mawu Ofanana  

Ndinati, Ndikadawauzira ndithu, ndikadafafaniza chikumbukiro chao mwa anthu.


Ndi chikhulupiriro Mose, atakula msinkhu, anakana kutchedwa mwana wake wa mwana wamkazi wa Farao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa