Machitidwe a Atumwi 7:20 - Buku Lopatulika20 Nyengo yomweyo anabadwa Mose, ndiye wokoma ndithu pamaso pa Mulungu; ndipo anamlera miyezi itatu m'nyumba ya atate wake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Nyengo yomweyo anabadwa Mose, ndiye wokoma ndithu pamaso pa Mulungu; ndipo anamlera miyezi itatu m'nyumba ya atate wake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Nthaŵi imeneyo Mose adabadwa, ndipo anali mwana wokongola kwambiri. Adamlera kwao miyezi itatu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Pa nthawi imeneyo Mose anabadwa, ndipo anali wokongola kwambiri. Iye analeredwa mʼnyumba ya abambo ake kwa miyezi itatu. Onani mutuwo |