Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:18 - Buku Lopatulika

18 kufikira inauka mfumu ina pa Ejipito, imene siinamdziwe Yosefe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 kufikira inauka mfumu ina pa Ejipito, imene siinamdziwa Yosefe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pambuyo pake mfumu ina imene sidadziŵe Yosefe, idayamba kulamulira ku Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Pambuyo pake mfumu yatsopano imene sinkamudziwa Yosefe, inayamba kulamulira dziko la Igupto.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:18
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo inalowa mfumu yatsopano mu ufumu wa Ejipito, imene siinadziwe Yosefe.


Imeneyo inachenjerera fuko lathu, niwachitira choipa makolo athu, niwatayitsa tiana tao, kuti tingakhale ndi moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa