Machitidwe a Atumwi 4:9 - Buku Lopatulika9 ngati ife lero tiweruzidwa chifukwa cha ntchito yabwino ya pa munthu wodwala, ndi machiritsidwe ake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 ngati ife lero tiweruzidwa chifukwa cha ntchito yabwino ya pa munthu wodwala, ndi machiritsidwe ake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 kodi mukutifunsa ife lero za ntchito yabwino imene idachitika pa munthu wopunduka uja, ndi kuchira kwake? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ngati ife tikufunsidwa lero chifukwa cha ntchito yabwino imene yachitika pa munthu wolumala miyendo ndi mmene iye anachiritsidwira, Onani mutuwo |