Machitidwe a Atumwi 4:6 - Buku Lopatulika6 ndi Anasi mkulu wa ansembe, ndi Kayafa, ndi Yohane, ndi Aleksandro, ndi onse amene anali a fuko la mkulu wa ansembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi Anasi mkulu wa ansembe, ndi Kayafa, ndi Yohane, ndi Aleksandro, ndi onse amene anali a fuko la mkulu wa ansembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kunalinso Anasi mkulu wa ansembe onse, pamodzi ndi Kayafa, Yohane, Aleksandro ndi ena onse a kubanja kwa mkulu wa ansembe onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Panali Anasi, Mkulu wa ansembe, Kayafa, Yohane ndi Alekisandro ndi ana a banja la mkulu wa ansembe. Onani mutuwo |