Machitidwe a Atumwi 4:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo m'mene anawaimika pakati, anafunsa kuti, Ndi mphamvu yanji, kapena m'dzina lanji, mwachita ichi inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo m'mene anawaimika pakati, anafunsa kuti, Ndi mphamvu yanji, kapena m'dzina lanji, mwachita ichi inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono adaimiritsa Petro ndi Yohane pakati pao naŵafunsa kuti, “Kodi zija mudachitazi, mudazichita ndi mphamvu yanji, kaya mudazichita m'dzina la yani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iwo anayimiritsa Petro ndi Yohane patsogolo pawo nayamba kuwafunsa kuti, “Kodi munachita zimenezi ndi mphamvu yanji kapena mʼdzina la yani?” Onani mutuwo |