Machitidwe a Atumwi 4:20 - Buku Lopatulika20 pakuti sitingathe ife kuleka kulankhula zimene tinaziona ndi kuzimva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 pakuti sitingathe ife kuleka kulankhula zimene tinaziona ndi kuzimva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ife ndiye sitingaleke kulankhula za zimene tidaziwona ndi kuzimva.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ife sitingaleke kuyankhula za zimene tinaziona ndi kuzimva.” Onani mutuwo |