Machitidwe a Atumwi 4:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anawaitana, nawalamulira kuti asanene konse kapena kuphunzitsa m'dzina la Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anawaitana, nawalamulira kuti asanene konse kapena kuphunzitsa m'dzina la Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Atatero adaŵaitana, naŵalamula kuti asatchule konse kapena kuphunzitsa za dzina la Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamenepo anawayitananso ndipo anawalamula kuti asayankhule kapena kuphunzitsa konse mʼdzina la Yesu. Onani mutuwo |