Machitidwe a Atumwi 4:1 - Buku Lopatulika1 Koma m'mene analikulankhula ndi anthu, ansembe ndi mdindo wa ku Kachisi ndi Asaduki anadzako, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma m'mene analikulankhula ndi anthu, ansembe ndi mdindo wa ku Kachisi ndi Asaduki anadzako, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Petro ndi Yohane akulankhulabe ndi anthu aja, kudadza ansembe ena pamodzi ndi mkulu wa asilikali a ku Nyumba ya Mulungu, ndi Asaduki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pamene Petro ndi Yohane amayankhula ndi anthu, kunabwera ansembe, mkulu woyangʼanira Nyumba ya Mulungu ndiponso Asaduki. Onani mutuwo |