Machitidwe a Atumwi 3:26 - Buku Lopatulika26 Kuyambira ndi inu, Mulungu, ataukitsa Mwana wake, anamtuma kukudalitsani inu, ndi kukubwezani yense ku zoipa zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kuyambira ndi inu, Mulungu, ataukitsa Mwana wake, anamtuma kukudalitsani inu, ndi kukubwezani yense ku zoipa zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Choncho Mulungu atasankhula Mtumiki wake adayamba kumtuma kwa inu, kuti akudalitseni pakuthandiza aliyense mwa inu kusiya njira zake zoipa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Pamene Mulungu anaukitsa mtumiki wake, anamutuma Iye poyamba kwa inu kuti akudalitseni pobweza aliyense wa inu ku zoyipa zake.” Onani mutuwo |