Machitidwe a Atumwi 3:13 - Buku Lopatulika13 Mulungu wa Abrahamu, ndi Isaki, ndi Yakobo, Mulungu wa makolo athu, analemekeza Mwana wake Yesu; amene inu munampereka ndi kumkaniza pa Pilato, poweruza iyeyu kummasula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mulungu wa Abrahamu, ndi Isaki, ndi Yakobo, Mulungu wa makolo athu, analemekeza Mwana wake Yesu; amene inu munampereka ndi kumkaniza pa Pilato, poweruza iyeyu kummasula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Iyai, koma Mulungu wa makolo athu, Abrahamu, Isaki ndi Yakobe, adapereka ulemerero kwa Yesu, Mtumiki wake. Inu mudampereka kwa adani ake ndi kumkana pamaso pa Pilato, pamene Pilatoyo adaatsimikiza kuti ammasula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mulungu wa Abrahamu, Isake ndi Yakobo, Mulungu wa makolo athu, wamulemekeza mtumiki wake Yesu. Amene inu munamukana pamaso pa Pilato ndi kumupereka Iye kuti aphedwe, ngakhale kuti Pilato anafuna kuti amumasule. Onani mutuwo |