Machitidwe a Atumwi 3:14 - Buku Lopatulika14 Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Yesu anali woyera mtima ndi wolungama, koma inu mudamkana, ndipo m'malo mwake mudapempha kuti akumasulireni chigaŵenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma inu munamukana Woyera ndi Wolungamayo ndipo munapempha kuti akumasulireni munthu wakupha anthu. Onani mutuwo |