Machitidwe a Atumwi 26:9 - Buku Lopatulika9 Inedi ndinayesa ndekha, kuti kundiyenera kuchita zinthu zambiri zotsutsana nalo dzina la Yesu Mnazarayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Inedi ndinayesa ndekha, kuti kundiyenera kuchita zinthu zambiri zotsutsana nalo dzina la Yesu Mnazarayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Ine ndemwe ndinkaganiza kuti ndinkayenera kuchita zinthu zambiri pofuna kuthetsa mbiri ya Yesu wa ku Nazarete. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Inenso ndimaganiza kuti ndimayenera kuchita zinthu zambiri pofuna kuthana ndi dzina la Yesu wa ku Nazareti. Onani mutuwo |