Machitidwe a Atumwi 26:8 - Buku Lopatulika8 Muchiyesa chinthu chosakhulupirika, chakuti Mulungu aukitsa akufa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Muchiyesa chinthu chosakhulupirika, chakuti Mulungu aukitsa akufa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Bwanji ena mwa inu Ayuda mumayesa kuti nkosatheka kukhulupirira kuti Mulungu nkuukitsa anthu kwa akufa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nʼchifukwa chiyani ena a inu mukuganiza kuti nʼkosatheka kuti Mulungu aukitse akufa? Onani mutuwo |