Machitidwe a Atumwi 26:4 - Buku Lopatulika4 Mayendedwe a moyo wanga tsono, kuyambira pa chibwana changa, amene anakhala chiyambire mwa mtundu wanga mu Yerusalemu, awadziwa Ayuda onse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mayendedwe a moyo wanga tsono, kuyambira pa chibwana changa, amene anakhala chiyambire mwa mtundu wanga m'Yerusalemu, awadziwa Ayuda onse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Ayuda onse akudziŵa za moyo wanga wonse kuyambira ndili mwana. Akudziŵa m'mene ndinkakhalira chiyambire pakati pa anthu a mtundu wanga, ndiponso ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Ayuda onse akudziwa za moyo wanga mmene ndakhalira kuyambira ndili mwana, kuchokera pachiyambi cha moyo wanga mʼdziko lathu ndiponso mu Yerusalemu. Onani mutuwo |