Machitidwe a Atumwi 26:2 - Buku Lopatulika2 Ndidziyesera wamwai, Mfumu Agripa, popeza nditi ndidzikanira lero pamaso panu, za zonse zimene Ayuda andinenera nazo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidziyesera wamwai, Mfumu Agripa, popeza nditi ndidzikanira lero pamaso panu, za zonse zimene Ayuda andinenera nazo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Inu Mfumu Agripa, ine ndikuganiza kuti ndine wamwai kuti ndi pamaso panu pamene ndiyankhe lero zonse zimene Ayuda akhala akundineneza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Mfumu Agripa ine ndikudziyesa wa mwayi kuyima pamaso panu lero lino ndi kudziteteza, kutsutsa zonse zimene Ayuda andinenera, Onani mutuwo |