Machitidwe a Atumwi 23:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo mkulu wa ansembe Ananiya analamulira akuimirirako ampande pakamwa pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo mkulu wa ansembe Ananiya analamulira akuimirirako ampande pakamwa pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Apo Ananiya, mkulu wa ansembe onse, adalamula amene adaaimirira pafupi ndi Paulo kuti, “Mtchayeni kukamwako!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Chifukwa cha mawu amenewa, mkulu wa ansembe Ananiya analamulira amene anali pafupi ndi Paulo kuti amumenye pakamwa. Onani mutuwo |