Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 22:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamve mau akulankhula nane.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamva mau akulankhula nane.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Anzanga apaulendo adaakuwona kuŵalako, koma mau a amene ankalankhula naneyo sadaŵamve.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Anzanga a paulendo anaona kuwalako, koma sanamve mawuwo, a Iye amene amayankhula nane.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 22:9
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ine Daniele ndekha ndinaona masomphenyawo; pakuti anthu anali nane sanaone masomphenyawo; koma kunawagwera kunjenjemera kwakukulu, nathawa kubisala.


dzuwa lamsana, ndinaona panjira, Mfumu, kuunika kochokera kumwamba kowalitsa koposa dzuwa kunawala pondizinga ine ndi iwo akundiperekeza.


Ndipo amunawo akumperekeza iye anaima duu, atamvadi mau, koma osaona munthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa