Machitidwe a Atumwi 22:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ndinayankha, Ndinu yani Mbuye? Ndipo anati kwa ine, Ndine Yesu wa ku Nazarete, amene umlondalonda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ndinayankha, Ndinu yani Mbuye? Ndipo anati kwa ine, Ndine Yesu wa ku Nazarete, amene umlondalonda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ine ndidafunsa kuti, ‘Ndinu yani, Ambuye?’ Ndipo iwo adati, ‘Ine ndine Yesu wa ku Nazarete, amene iwe ukumzunza.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ine ndinafunsa kuti, “Ndinu ndani Ambuye?” Iye anayankha kuti, “Ndine Yesu wa ku Nazareti, amene iwe ukumuzunza.” Onani mutuwo |