Machitidwe a Atumwi 22:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo ndinagwa pansitu, ndipo ndinamva mau akunena nane, Saulo, Saulo, undilondalonderanji Ine? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo ndinagwa pansitu, ndipo ndinamva mau akunena nane, Saulo, Saulo, undilondalonderanji Ine? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndidagwa pansi kenaka ndidamva mau onena kuti, ‘Saulo, Saulo, ukundizunziranji?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndinagwa pansi ndipo ndinamva mawu akuti, ‘Saulo! Saulo! Ukundizunziranji?’ ” Onani mutuwo |