Machitidwe a Atumwi 22:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo kunali, pakupita ine ndi kuyandikira ku Damasiko, monga usana, mwadzidzidzi kunandiwalira pondizungulira ine kuunika kwakukulu kochokera kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo kunali, pakupita ine ndi kuyandikira ku Damasiko, monga usana, mwadzidzidzi kunandiwalira pondizungulira ine kuunika kwakukulu kochokera kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Pamene ndinali pa ulendowo ndi kuyandikira Damasiko, nthaŵi ili ngati 12 koloko yamasana, mwadzidzidzi kuŵala kwakukulu kochokera kumwamba kudandizinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Nthawi ya masana, nditayandikira ku Damasiko, mwadzidzidzi kuwala kwakukulu kochokera kumwamba kunandizungulira. Onani mutuwo |