Machitidwe a Atumwi 22:4 - Buku Lopatulika4 ndipo ndinalondalonda Njira iyi kufikira imfa, ndi kumanga ndi kupereka kundende amuna ndi akazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndipo ndinalondalonda Njira iyi kufikira imfa, ndi kumanga ndi kupereka kundende amuna ndi akazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndinkazunza anthu otsata Njira Yatsopanoyi, mpaka kumaŵapha. Ndinkaŵagwira anthuwo amuna ndi akazi omwe, nkumaŵamangitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine ndinkazunza anthu otsatira Njirayi mpaka kuwapha. Ndinkagwira amuna ndi amayi ndi kuwayika mʼndende. Onani mutuwo |