Machitidwe a Atumwi 20:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anamperekeza kufikira ku Asiya Sopatere mwana wa Piro, wa ku Berea; ndipo a Atesalonika, Aristariko ndi Sekundo; ndi Gayo wa ku Deribe, ndi Timoteo; ndi a ku Asiya, Tikiko ndi Trofimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anamperekeza kufikira ku Asiya Sopatere mwana wa Piro, wa ku Berea; ndipo a Atesalonika, Aristariko ndi Sekundo; ndi Gayo wa ku Deribe, ndi Timoteo; ndi a ku Asiya, Tikiko ndi Trofimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adamperekeza ndi Sopatere, mwana wa Piro, wa ku Berea; Aristariko ndi Sekundo a ku Tesalonika; Gayo wa ku Deribe; Timoteo; ndi Tikiko ndi Trofimo a ku Asiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anapita pamodzi ndi Sopatro mwana wa Puro wa ku Bereya, Aristariko ndi Sekundo a ku Tesalonika, Gayo wa ku Derbe ndi Timoteyo, ndipo a ku Asiya anali Tukiko ndi Trofimo. Onani mutuwo |