Machitidwe a Atumwi 20:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo m'mene adakhalako miyezi itatu, ndipo atampangira chiwembu Ayuda, poti iye apite ndi ngalawa ku Siriya, anatsimikiza mtima abwerere popyola Masedoniya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo m'mene adakhalako miyezi itatu, ndipo atampangira chiwembu Ayuda, poti iye apite ndi ngalawa ku Siriya, anatsimikiza mtima abwerere popyola Masedoniya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 nakakhalako miyezi itatu. Pamene anali pafupi kupita ku Siriya pa chombo, Ayuda adamchita chiwembu. Tsono iye adatsimikiza zodzera ku Masedoniya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kumeneko anakhala miyezi itatu. Popeza kuti Ayuda anakonza zomuchita chiwembu pamene amati azinyamuka kupita ku Siriya pa sitima ya pamadzi, iye anaganiza zobwereranso kudzera ku Makedoniya. Onani mutuwo |