Machitidwe a Atumwi 18:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anafotokozera m'sunagoge masabata onse, nakopa Ayuda ndi Agriki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anafotokozera m'sunagoge masabata onse, nakopa Ayuda ndi Agriki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pa tsiku la Sabata lililonse iye ankakambirana ndi anthu ku nyumba yamapemphero ya Ayuda, namayesetsa kukopa Ayuda ndi Agriki omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsiku la Sabata lililonse Paulo amakambirana ndi anthu mʼsunagoge, kufuna kukopa Ayuda ndi Agriki. Onani mutuwo |