Machitidwe a Atumwi 18:5 - Buku Lopatulika5 Koma pamene Silasi ndi Timoteo anadza potsika ku Masedoniya, Paulo anapsinjidwa ndi mau, nachitira umboni kwa Ayuda kuti Yesu ndiye Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma pamene Silasi ndi Timoteo anadza potsika ku Masedoniya, Paulo anapsinjidwa ndi mau, nachitira umboni kwa Ayuda kuti Yesu ndiye Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Silasi ndi Timoteo atafika kuchokera ku Masedoniya, Paulo tsopano ankangogwira ntchito yolalikira, ndi kuŵauza Ayuda monenetsa kuti Yesu ndiye anali Mpulumutsi wolonjezedwa uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Sila ndi Timoteyo atafika kuchokera ku Makedoniya, Paulo ankangogwira ntchito yolalikira yokha basi, kuchitira umboni Ayuda kuti Yesu ndiye Khristu. Onani mutuwo |