Machitidwe a Atumwi 12:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo anatuluka, namtsata; ndipo sanadziwe kuti nchoona chochitidwa ndi mngelo, koma anayesa kuti alikuona masomphenya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo anatuluka, namtsata; ndipo sanadziwa kuti nchoona chochitidwa ndi mngelo, koma anayesa kuti alikuona masomphenya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo Petro adatuluka namtsata, osazindikira kuti zimene mngelo ankachitazo nzoona. Ankangoyesa kuti akuwona zinthu m'masomphenya chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Petro anatsatira natuluka mʼndende, koma sanazindikire kuti zimene mngeloyo amachita zimachitikadi; iye amaganiza kuti amaona masomphenya. Onani mutuwo |