Machitidwe a Atumwi 11:8 - Buku Lopatulika8 Koma ndinati, Iaitu, Ambuye; pakuti kanthu wamba, kapena konyansa sikanalowe m'kamwa mwanga ndi kale lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma ndinati, Iaitu, Ambuye; pakuti kanthu wamba, kapena konyansa sikanalowe m'kamwa mwanga ndi kale lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma ine ndidati, ‘Iyai pepani Ambuye, ine ndi kale lonse chinthu chosayera kapena chonyansa sichinaloŵepo pakamwa pangapa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Ine ndinayankha kuti, ‘Ayi, Ambuye! Pakuti chinthu chodetsedwa ndi chonyansa sindinadyepo pakamwa pangapa.’ Onani mutuwo |