Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 11:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Tsono ndidamva mau ondiwuza kuti, ‘Petro dzuka, ipha, udye.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kenaka ine ndinamva mawu akuti, ‘Petro, Imirira. Ipha, nudye.’

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 11:7
3 Mawu Ofanana  

chimenecho ndidachipenyetsetsa ndinachilingirira, ndipo ndinaona nyama za miyendo inai za padziko ndi zilombo, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga.


Koma ndinati, Iaitu, Ambuye; pakuti kanthu wamba, kapena konyansa sikanalowe m'kamwa mwanga ndi kale lonse.


Pakuti cholengedwa chonse cha Mulungu nchabwino, ndipo palibe kanthu kayenera kutayika, ngati kalandiridwa ndi chiyamiko;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa