Machitidwe a Atumwi 11:6 - Buku Lopatulika6 chimenecho ndidachipenyetsetsa ndinachilingirira, ndipo ndinaona nyama za miyendo inai za padziko ndi zilombo, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 chimenecho ndidachipenyetsetsa ndinachilingirira, ndipo ndinaona nyama za miyendo inai za padziko ndi zilombo, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Nditachipenyetsetsa, ndidaonamo nyama zoŵeta ndi zakuthengo ndiponso zokwaŵa ndi mbalame zamumlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine ndinayangʼana mʼkati mwake ndipo ndinaona nyama za miyendo inayi za mʼdziko lapansi, zirombo, zokwawa, ndi mbalame zamlengalenga. Onani mutuwo |