Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 10:18 - Buku Lopatulika

18 ndipo anaitana nafunsa ngati Simoni, wotchedwanso Petro, acherezedwako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 ndipo anaitana nafunsa ngati Simoni, wotchedwanso Petro, acherezedwako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adaitana nkufunsa kuti, “Kodi kuli mlendo kuno, dzina lake Simoni, wotchedwanso Petro?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Iwo anayitana nafunsa ngati Simoni amene amadziwika ndi dzina loti Petro amakhala kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 10:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pokayikakayika Petro mwa yekha ndi kuti masomphenya adawaona akuti chiyani, taonani, amuna aja otumidwa ndi Kornelio, atafunsira nyumba ya Simoni, anaima pachipata,


Ndipo m'mene Petro analingirira za masomphenya, Mzimu anenana naye, Taona, amuna atatu akufuna iwe.


Ndipo taonani, pomwepo amuna atatu anaima pa khomo la nyumba m'mene munali ife, anatumidwa kwa ine ochokera ku Kesareya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa