Machitidwe a Atumwi 10:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo m'mene Petro analingirira za masomphenya, Mzimu anenana naye, Taona, amuna atatu akufuna iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo m'mene Petro analingirira za masomphenya, Mzimu anenana naye, Taona, amuna atatu akufuna iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pamene Petro ankalingalirabe za zimene adaaziwona m'masomphenya zija, Mzimu Woyera adamuuza kuti, “Iwe, anthu atatu akukufuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Petro akuganizirabe za masomphenyawo, Mzimu Woyera anati kwa iye, “Simoni, anthu atatu akukufunafuna. Onani mutuwo |