Machitidwe a Atumwi 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo m'mene adanena izi, ali chipenyerere iwo, ananyamulidwa; ndipo mtambo unamlandira Iye kumchotsa kumaso kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo m'mene adanena izi, ali chipenyerere iwo, ananyamulidwa; ndipo mtambo unamlandira Iye kumchotsa kumaso kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Atanena zimenezi, Yesu adatengedwa kupita Kumwamba, iwo akupenya. Ndipo mtambo udamlandira nkumubisa, iwo osamuwonanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Atatha kuyankhula zimenezi, Yesu anatengedwa kupita kumwamba ophunzira ake akuona, ndipo anabisika mʼmitambo. Onani mutuwo |