Luka 9:52 - Buku Lopatulika52 natumiza amithenga patsogolo pake; ndipo ananka, nalowa m'mudzi wa Asamariya, kukamkonzera Iye malo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 natumiza amithenga patsogolo pake; ndipo ananka, nalowa m'mudzi wa Asamariya, kukamkonzera Iye malo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Motero adatuma amithenga kuti atsogole, akaloŵe m'mudzi wina wa Asamariya kukamkonzera malo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 ndipo anatuma nthumwi kuti zitsogole. Iwo anapita mʼmudzi wa Asamariya kuti akonzekere kumulandira, Onani mutuwo |