Luka 9:51 - Buku Lopatulika51 Ndipo panali, pamene anayamba kukwanira masiku akuti alandiridwe Iye kumwamba, Yesu anatsimikiza kuloza nkhope yake kunka ku Yerusalemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Ndipo panali, pamene anayamba kukwanira masiku akuti alandiridwe Iye kumwamba, Yesu anatsimikiza kuloza nkhope yake kunka ku Yerusalemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Pamene masiku ankayandikira oti Yesu atengedwe kunka Kumwamba, Iye adatsimikiza ndithu zopita ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Nthawi itayandikira yoti Iye atengedwe kupita kumwamba, Yesu anatsimikiza zopita ku Yerusalemu, Onani mutuwo |