Luka 9:50 - Buku Lopatulika50 Koma Yesu anati kwa iye, Musamletse, pakuti iye amene satsutsana nanu athandizana nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Koma Yesu anati kwa iye, Musamletse, pakuti iye amene satsutsana nanu athandizana nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Koma Yesu adamuuza kuti, “Musamletse ai, chifukwa wosatsutsana nanu, ngwogwirizana nanu ameneyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Yesu anati, “Wosamuletsa, pakuti amene satsutsana nanu ali mbali yanu.” Onani mutuwo |