Luka 9:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Ndinapempha ophunzira anuŵa kuti autulutse, koma alephera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Ine ndinapempha ophunzira anu kuti achitulutse, koma alephera.” Onani mutuwo |