Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Ndinapempha ophunzira anuŵa kuti autulutse, koma alephera.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Ine ndinapempha ophunzira anu kuti achitulutse, koma alephera.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:40
7 Mawu Ofanana  

Nawatsogolera Gehazi, naika ndodo pankhope pa mwanayo; koma mwanayo analibe mau, kapena kusamalira. Motero anabwerera kukomana naye, namuuza kuti, Sanauke mwanayo.


Ndipo Iye ananena kwa iwo, Chifukwa chikhulupiriro chanu nchaching'ono: pakuti indetu ndinena kwa inu, Mukakhala nacho chikhulupiriro monga kambeu kampiru, mudzati ndi phiri ili, Senderapo umuke kuja; ndipo lidzasendera; ndipo palibe kanthu kadzakukanikani.


Ndipo Iye anaitana pamodzi khumi ndi awiriwo nawapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse, ndi zakuchiritsa nthenda.


ndipo onani, umamgwira iye mzimu, nafuula modzidzimuka; ndipo umamng'amba iye ndi kumchititsa thovu pakamwa, suchoka pa iye, koma umsautsa koopsa.


Ndipo Yesu anayankha, nati, Ha! Obadwa inu osakhulupirira ndi amphulupulu, ndidzakhala ndi inu nthawi yanji, ndi kulekerera inu? Idza naye kuno mwana wako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa