Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo onani, analikulankhulana naye amuna awiri, ndiwo Mose ndi Eliya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo onani, analikulankhulana naye amuna awiri, ndiwo Mose ndi Eliya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Nthaŵi yomweyo anthu aŵiri adayamba kucheza naye; anali Mose ndi Eliya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Anthu awiri, Mose ndi Eliya,

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:30
13 Mawu Ofanana  

Ndipo adzamtsogolera Iye, ndi mzimu ndi mphamvu ya Eliya, kutembenuzira mitima ya atate kwa ana ao, ndi osamvera kuti atsate nzeru ya olungama mtima; kukonzeratu Ambuye anthu okonzeka.


Ndipo anayamba kwa Mose, ndi kwa aneneri onse nawatanthauzira iwo m'malembo onse zinthu za Iye yekha.


Ndipo anati kwa iwo, Awa ndi mauwo ndinalankhula nanu, paja ndinakhala ndi inu, kuti ziyenera kukwanitsidwa zonse zolembedwa za Ine m'chilamulo cha Mose, ndi aneneri, ndi Masalimo.


Ndipo anayankha nati, Yohane Mbatizi; koma ena, Eliya; ndi ena, kuti anauka mmodzi wa aneneri akale.


Ndipo m'kupemphera kwake, maonekedwe a nkhope yake anasandulika, ndi chovala chake chinayera ndi kunyezimira.


amene anaonekera mu ulemerero, nanena za kumuka kwake kumene Iye ati adzatsiriza ku Yerusalemu.


Chifukwa chilamulo chinapatsidwa mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinadza mwa Yesu Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa