Luka 9:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo onani, analikulankhulana naye amuna awiri, ndiwo Mose ndi Eliya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo onani, analikulankhulana naye amuna awiri, ndiwo Mose ndi Eliya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Nthaŵi yomweyo anthu aŵiri adayamba kucheza naye; anali Mose ndi Eliya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Anthu awiri, Mose ndi Eliya, Onani mutuwo |