Luka 9:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo m'kupemphera kwake, maonekedwe a nkhope yake anasandulika, ndi chovala chake chinayera ndi kunyezimira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo m'kupemphera kwake, maonekedwe a nkhope yake anasandulika, ndi chovala chake chinayera ndi kunyezimira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Pamene Iye ankapemphera, maonekedwe a nkhope yake adasandulika, ndipo zovala zake zidachita kuti mbee kuyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Pamene Iye ankapemphera, maonekedwe a nkhope yake, ndi zovala zake zinawala monyezimira kwambiri. Onani mutuwo |