Luka 9:27 - Buku Lopatulika27 Koma Ine ndinena ndi inu zoonadi, Kuli ena a iwo akuimirira pano, amene sadzalawatu imfa, kufikira kuti adzaona Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma Ine ndinena ndi inu zoonadi, Kuli ena a iwo akuimirira pano, amene sadzalawatu imfa, kufikira kuti adzaona Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma ndithu ndikunenetsa kuti alipo ena pompano omwe sadzafa asanaone Ufumu wa Mulungu utafika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti ena mwa inu amene mwayima pano simudzalawa imfa musanaone ufumu wa Mulungu.” Onani mutuwo |