Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:14 - Buku Lopatulika

14 Pakuti anali amuna ngati zikwi zisanu. Koma Iye anati kwa ophunzira ake, Khalitsani iwo pansi magulumagulu, ngati makumi asanuasanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pakuti anali amuna ngati zikwi zisanu. Koma Iye anati kwa ophunzira ake, Khalitsani iwo pansi magulumagulu, ngati makumi asanuasanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ndiye kuti amuna okha adaalipo ngati zikwi zisanu. Tsono Yesu adauza ophunzira ake kuti, “Auzeni anthuŵa akhale pansi m'magulumagulu, gulu lililonse anthu ngati makumi asanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 (Pamenepo panali amuna pafupifupi 5,000). Koma Iye anati kwa ophunzira ake, “Akhazikeni pansi mʼmagulu a anthu pafupifupi makumi asanu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:14
5 Mawu Ofanana  

Ndipo analamulira anthu a khamulo akhale pansi; natenga mikate isanu ndi iwiriyo, nayamika, nanyema, napatsa ophunzira ake, kuti apereke kwa iwo; ndipo anapereka kwa khamulo.


Koma anati kwa iwo, Muwapatse chakudya ndinu. Koma anati, Ife tilibe mikate, koma isanu yokha, ndi nsomba ziwiri zokha; kapena timuke ife kukagulira anthu awa onse zakudya.


Ndipo anatero, nawakhalitsa pansi onsewo.


Koma zonse zichitike koyenera ndi kolongosoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa