Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anatero, nawakhalitsa pansi onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anatero, nawakhalitsa pansi onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Ophunzira aja adaŵakhalitsadi anthu onse aja pansi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ophunzira ake anachita zomwezo ndipo aliyense anakhala pansi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:15
2 Mawu Ofanana  

Pakuti anali amuna ngati zikwi zisanu. Koma Iye anati kwa ophunzira ake, Khalitsani iwo pansi magulumagulu, ngati makumi asanuasanu.


Ndipo Iye, m'mene anatenga mikate isanu ija ndi nsomba ziwiri anayang'ana kumwamba, nazidalitsa, nanyema, napatsa ophunzira apereke kwa anthuwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa