Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:53 - Buku Lopatulika

53 Ndipo anamseka Iye pwepwete podziwa kuti anafa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 Ndipo anamseka Iye pwepwete podziwa kuti anafa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Pamenepo anthuwo adayamba kumseka monyodola, chifukwa ankadziŵa kuti mwanayo wamwalira basi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Iwo anamuseka podziwa kuti anali atamwalira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:53
11 Mawu Ofanana  

Ndine ngati munthu wosekedwa ndi mnansi wake, ndinaitana kwa Mulungu, ndipo anandiyankha; munthu wolungama wangwiro asekedwa.


Zoonadi, ali nane ondiseka; ndi diso langa lili chipenyere m'kundiwindula kwao.


Onse akundipenya andiseka; akwenzula, apukusa mutu, nati,


Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu; munthu wazisoni, ndi wodziwa zowawa; ndipo ananyozedwa monga munthu wombisira anthu nkhope zao; ndipo ife sitinamlemekeze.


ananena, Tulukani, pakuti kabuthuko sikanafe koma kali m'tulo. Ndipo anamseka Iye pwepwete.


Koma Afarisi, ndiwo okonda ndalama, anamva izi zonse; ndipo anamseka.


Ndipo anthu onse analikumlira iye ndi kudziguguda pachifuwa. Koma Iye anati, Musalire; pakuti iye sanafe, koma wagona tulo.


Ndipo Iye anamgwira dzanja lake, naitana, nati, Buthu, tauka.


Yesu ananena, Chotsani mwala. Marita, mlongo wake wa womwalirayo, ananena ndi Iye, Ambuye, adayamba kununkha: pakuti wagona masiku anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa