Luka 8:53 - Buku Lopatulika53 Ndipo anamseka Iye pwepwete podziwa kuti anafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Ndipo anamseka Iye pwepwete podziwa kuti anafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Pamenepo anthuwo adayamba kumseka monyodola, chifukwa ankadziŵa kuti mwanayo wamwalira basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Iwo anamuseka podziwa kuti anali atamwalira. Onani mutuwo |